Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili M‘buku la Hagai

HAGAI

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Anadzudzula anthu chifukwa chosamanganso kachisi (1-11)

      • ‘Kodi ino ndi nthawi yoti inu muzikhala mʼnyumba zokongoletsedwa ndi matabwa?’ (4)

      • “Ganizirani mofatsa zimene mukuchita” (5)

      • Kudzala zambiri nʼkukolola zochepa (6)

    • Anthu anamvera mawu a Yehova (12-15)

  • 2

    • Kachisi wachiwiri adzadzaza ndi ulemerero (1-9)

      • Kugwedeza mitundu yonse ya anthu (7)

      • Zinthu zamtengo wapatali zochokera ku mitundu ya anthu zidzabwera (7)

    • Madalitso obwera chifukwa chomanganso kachisi (10-19)

      • Chopatulika sichingachititse kuti chodetsedwa chikhale chopatulika (10-14)

    • Uthenga wopita kwa Zerubabele (20-23)

      • “Ndidzachititsa kuti ukhale ngati mphete yodindira” (23)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani