Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili Mʼbuku la 2 Petulo

2 PETULO

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Moni (1)

    • Mupitirizebe kukhala pakati pa anthu oitanidwa (2-15)

      • Makhalidwe ofunika kuwonjezera pa chikhulupiriro (5-9)

    • Mawu aulosi adzakwaniritsidwa (16-21)

  • 2

    • Kudzakhala aphunzitsi abodza (1-3)

    • Umboni wotsimikizira kuti aphunzitsi abodza adzaweruzidwa (4-10a)

      • Angelo anawaponya mu Tatalasi (4)

      • Chigumula; Sodomu ndi Gomora (5-7)

    • Mmene tingadziwire aphunzitsi abodza (10b-22)

  • 3

    • Anthu onyoza amakayikira zoti anthu oipa adzawonongedwa (1-7)

    • Yehova sakuchedwa (8-10)

    • Ganizirani za mtundu wa anthu amene muyenera kukhala (11-16)

      • Kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano (13)

    • Chenjerani kuti anthu asakusocheretseni (17, 18)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani