Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.05 2
  • May 7-13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 7-13
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.05 2

May 7-13

MALIKO 7-8

  • Nyimbo Na. 13 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Nyamula Mtengo Wako Wozunzikirapo, ndi Kunditsatira Mosalekeza”: (10 min.)

    • Maliko 8:34​—Kuti tikhale wotsatira wa Yesu tiyenera kudzikana tokha (“adzikane yekha” mfundo zimene ndikuphunzira pa Maliko 8:34, nwtsty; w92 8/1 17 ¶14)

    • Maliko 8:35-37​—Yesu anafunsa mafunso awiri ofunika amene angatithandize kuti tiziika zinthu zofunika kwambiri pa malo oyamba (w08 10/15 25-26 ¶3-4)

    • Maliko 8:38​—Pamafunika kulimba mtima kuti tikhale otsatira a Khristu (jy 143 ¶4)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Maliko 7:5-8​—N’chifukwa chiyani kusamba m’manja inali nkhani yaikulu kwa Afarisi? (w16.08 30 ¶1-4)

    • Maliko 7:32-35​—Kodi tikuphunzirapo chiyani pa zimene Yesu anachita posonyeza kuganizira munthu wina wogontha? (w00 2/15 17-18 ¶9-11)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Maliko 7:1-15

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 165-166 ¶6-7

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 51

  • Zofunika Pampingo: (5 min.)

  • “Muzithandiza Ana Anu Kuti Akhale Otsatira a Khristu”: (10 min.) Nkhani yokambirana.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 17 ¶19-20 komanso tsamba 187, 188-191

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 60 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani