Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb20.03
  • Yakobo Analandira Madalitso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yakobo Analandira Madalitso
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Yakobo ndi Esau Akhululukirana
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Yakobo Analandira Madalitso
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Zimene Zili Mʼbuku la Genesis
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20.03
Yakobo wavala zovala za Esau komanso waika chikopa cha mbuzi m’khosi ndi m’mikono yake ndipo Isaki akukhudza mikono yake.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 27-28

Yakobo Analandira Madalitso

27:6-10, 18, 19, 27-29

Madalitso amene Yakobo analandira kuchokera kwa bambo ake, anali ulosi wa zimene zidzachitike m’tsogolo.

  • Mapu a Dziko Lolonjezedwa akusonyeza dera la Isiraeli lomwe ndi lobiriwira komanso lachonde mosiyana ndi dera la Edomu lomwe ndi louma kwambiri.

    27:28​—Yehova anapatsa mbadwa za Yakobo dziko lachonde “loyenda mkaka ndi uchi.”​—De 26:15

  • 27:29​—Aisiraeli (mbadwa za Yakobo) anadzakhala mtundu wamphamvu kuposa Aedomu (mbadwa za Esau).​—Ge 25:23; 2Sa 8:14

  • 27:29​—Aedomu anatembereredwa chifukwa ankadana ndi Aisiraeli ndipo patapita nthawi anawonongedwa.​—Eze 25:12-14

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani