Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 129
  • Tipitirizebe Kupirira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tipitirizebe Kupirira
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Muzitsanzira Yehova pa Nkhani ya Kupirira
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 129

NYIMBO 129

Tipitirizebe Kupirira

zosindikizidwa

(Mateyu 24:13)

  1. 1. Tizipirira

    Mayesero ngati Yesu.

    Anavutika

    Koma ankasangalala

    Ndi chiyembekezo.

    Analimba mtima.

    (KOLASI)

    Tikhale opirira.

    Tizilalikira.

    M’lungu amatikonda

    Adzatithandiza kupirira.

  2. 2. Tingakumane

    Ndi mavuto ochuluka,

    Tidikirebe

    Moyo wosatha m’tsogolo.

    Tikulakalaka

    Mtendere wosatha.

    (KOLASI)

    Tikhale opirira.

    Tizilalikira.

    M’lungu amatikonda

    Adzatithandiza kupirira.

  3. 3. Sitimaopa

    Kapena kukayikira.

    Titumikire

    Mpaka tsiku lomaliza.

    Tsiku la Yehova

    Lilidi pafupi.

    (KOLASI)

    Tikhale opirira.

    Tizilalikira.

    M’lungu amatikonda

    Adzatithandiza kupirira.

(Onaninso Mac. 20:​19, 20; Yak. 1:​12; 1 Pet. 4:​12-​14.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani