Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • wp21.1
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphero Athu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
  • Mmene Yehova Amayankhira Mapemphero Athu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Tili Ndi Mwayi Wopemphera kwa Mulungu
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
  • Pemphero Lingakuthandizeni Kuti Mulungu Akhale Mnzanu
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
wp21.1

Mawu Oyamba

Kodi munayamba mwaganizapo kuti Mulungu samva mapemphero anu? Ngati zili choncho, dziwani kuti si inu nokha. Anthu ambiri anapemphapo Mulungu kuti awathandize koma mavuto awo sanathe. Nkhani zotsatirazi ziyankha mafunso awa: Kodi n’chifukwa chiyani sitiyenera kukayikira kuti Mulungu amamva mapemphero athu? N’chifukwa chiyani mapemphero ena sayankhidwa? Nanga kodi tiyenera kuchita chiyani kuti mapemphero athu aziyankhidwa?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani