Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Ayuda ena ankadana ndi anthu ofufuta zikopa chifukwa ntchitoyi inkawachititsa kuti azigwira zikopa, nyama zakufa komanso ankagwiritsa ntchito zinthu zina zonyansa pogwira ntchitoyi. Anthu ofufuta zikopa ankaonedwa kuti ndi osayenera kufika pakachisi, ndipo malo awo ogwirira ntchito ankafunika kukhala kunja kwa mzinda pa mtunda pafupifupi mamita 20. Mwina chimenechi chinali chimodzi mwa zifukwa zimene zinachititsa kuti nyumba ya Simoni ikhale “m’mbali mwa nyanja.”​—Mac. 10:6.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani