Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

c Boazi anapatsa Rute balere wokwana miyezo 6. Mwina iye anachita zimenezi posonyeza kuti, mofanana ndi mmene zinkakhalira kuti masiku 6 ogwira ntchito ankatsatana ndi tsiku la Sabata limene linali lopuma, Rute yemwe anakhala nthawi yaitali ali wamasiye anali atatsala pang’ono ‘kupuma,’ kutanthauza kuti ankayembekezera kupeza mwamuna n’kukhala ndi nyumba yakeyake. Koma n’kuthekanso kuti Boazi anapatsa Rute miyezo 6 chifukwa ndi imene Ruteyo akanatha kunyamula.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani