Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Zikuoneka kuti mzinda wa Samariya, womwe unali likulu la dziko la Isiraeli, unali ndi anthu 20,000 kapena 30,000 m’nthawi ya Yona. Koma chiwerengerochi chinali chochepa kwambiri poyerekeza ndi chiwerengero cha anthu a ku Nineve. Pa nthawi imene mzinda wa Nineve unali wotukuka kwambiri, uyenera kuti unali waukulu kwambiri padziko lonse.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani