Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

b MATANTHAUZO A MAWU ENA: Kufatsa. Anthu ofatsa amakhala odekha pochita zinthu ndi anzawo ndipo sapsa mtima ngakhale ataputidwa. Kudzichepetsa. Anthu odzichepetsa sadzikuza kapena kudzitama ndipo amaona kuti anthu ena ndi owaposa. Yehova ndi wodzichepetsanso chifukwa ngakhale kuti ndi wamkulu kwambiri amachita zinthu ndi ena mwachikondi komanso mwachifundo.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani