Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Kudzozedwa ndi mzimu woyera: Yehova amagwiritsa ntchito mzimu wake woyera kusankha munthu kuti akalamulire ndi Yesu kumwamba. Pogwiritsa ntchito mzimu wake, Mulungu amapatsa munthuyo “chikole” kapena kuti kumulonjeza zinthu zam’tsogolo. (Aef. 1:13, 14) Akhristu amenewa anganene kuti mzimu woyera “umachitira umboni,” kapena kuti kuwatsimikizira kuti mphoto yawo ili kumwamba.​—Aroma 8:16.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani