Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

c MAWU OFOTOKOZERA CHITHUNZI: Zithunzi zitatu zosonyeza zimene zikuchitika misonkhano isanayambe, ikuchitika komanso itatha. 1: Mkulu akupereka moni mwansangala kwa mlendo, m’bale wachinyamata wanyamula maikofoni komanso mlongo wachitsikana akucheza ndi mlongo wachikulire. 2: Ana komanso achikulire akweza manja kuti ayankhe paphunziro la Nsanja ya Olonda. 3: Banja likugwira nawo ntchito yoyeretsa m’Nyumba ya Ufumu. Mayi akuthandiza mwana wake kuti aponye ndalama m’bokosi. M’bale wachinyamata akusamalira mabuku komanso m’bale wina akulimbikitsa mlongo wachikulire.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani