Mawu a M'munsi
a Monga mmene agwiritsidwira ntchito m’Malemba, mawu akuti ‘kuopa’ ali ndi matanthauzo ambiri. Mogwirizana ndi nkhani imene ikufotokozedwa, mawuwa angatanthauze mantha kapenanso ulemu. Nkhaniyi itithandiza kukhala ndi mantha omwe angatilimbikitse kukhala olimba mtima komanso okhulupirika potumikira Atate wathu wakumwamba.