Mawu a M'munsi
a Yehova ndi Yesu ndi ololera ndipo amafuna kuti ifenso tikhale ololera. Ngati ndife ololera, zidzakhala zosavuta kuvomereza zinthu zikasintha pa moyo wathu, monga pa nkhani yokhudza thanzi lathu kapena zachuma. Tidzalimbikitsanso mtendere ndi mgwirizano mumpingo.