Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Achinyamata amene akutumikira Yehova masiku ano amakumana ndi mavuto omwe amawayesa pa nkhani ya kulimba mtima komanso kukhalabe okhulupirika kwa Yehova. Anzawo a m’kalasi angamawanyoze chifukwa chokhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa. Kapenanso anzawo ena angawachititse kuti azidzimva kuti ndi opusa chifukwa chotumikira Mulungu komanso kutsatira mfundo zake. Koma munkhaniyi tiona kuti, anthu amene amatsanzira mneneri Danieli ndiponso kutumikira Yehova molimba mtima komanso mokhulupirika, ndi anzeru.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani