Mawu a M'munsi
a Munkhaniyi, tikambirana zimene Yehova ananena pofuna kutsimikizira kuti zimene analonjeza zokhudza Paradaiso zidzakwaniritsidwa. Nthawi iliyonse imene timauza anthu ena zimenezi, zimatithandiza ifenso kuti tizikhulupirira kwambiri malonjezo a Yehova.