Mawu a M'munsi
e MAWU OFOTOKOZERA CHITHUNZI: M’bale yemwe ali m’ndende chifukwa cha chikhulupiriro chake akuganizira mmene Yehova anamuthandizira kuti asiye kusuta, mmene akumulimbikitsira kudzera m’makalata ochokera kwa abale ndi alongo ake komanso moyo wosatha womwe adzamupatse m’Paradaiso.