Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Pa Deuteronomo 23:3-6, lamulo la Mulungu linkanena kuti a Amoni ndi a Mowabu asamalowe mu mtundu wa Aisiraeli. Koma zikuoneka kuti lamuloli linkaletsa kuti anthu a mitundu imeneyi asamavomerezedwe mwalamulo kukhala Aisiraeli, koma silinkawaletsa kuchita zinthu ndi Aisiraeli kapenanso kukhala pakati pawo. Onani buku la Insight on the Scriptures, Voliyumu 1, tsamba 95.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani