Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Ngakhale Yobu, yemwe anali wokhulupirika, anasokonezeka ataganizira mmene anzake atatu ankamuonera. Poyamba, ana ake onse atamwalira komanso katundu wake yense atawonongeka, “Yobu sanachimwe kapena kuimba Mulungu mlandu woti wachita zinthu zoipa.” (Yobu 1:22; 2:10) Koma pambuyo pake, anzakewo atamunena kuti Yobu wachita zinazake zoipa, anayamba ‘kulankhula mosaganiza bwino.’ Iye ankaona kuti chofunika kwambiri ndi kuteteza mbiri yake kuposa kuyeretsa dzina la Mulungu.—Yobu 6:3; 13:​4, 5; 32:2; 34:5.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani