Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Tyndale anagwiritsa ntchito dzina lakuti “Iehouah” pomasulira mabuku 5 oyambambirira a m’Baibulo. Patapita nthawi Chingelezi chinasintha ndipo dzina la Mulungu anayamba kulilemba mogwirizana ndi mmene anthu ankalankhulira pa nthawiyo. Mwachitsanzo, mu 1612, Henry Ainsworth anagwiritsa ntchito dzina lakuti “Iehovah” pomasulira buku lonse la Masalimo. Koma pamene ankakonzanso Baibuloli mu 1639, anagwiritsa ntchito dzina lakuti “Yehova.” Nawonso omasulira Baibulo la American Standard Version, anagwiritsa ntchito dzina lakuti “Yehova” m’malo onse amene dzina la Mulungu linkapezeka m’malemba a Chiheberi.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani