Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 130
  • Muzikhululuka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzikhululuka
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amadalitsa Anthu Omwe Amakhululuka
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Tingatsanzire Bwanji Kukhululuka kwa Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
  • Yehova Amakhululuka Kwambiri Kuposa Aliyense
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 130

NYIMBO 130

Muzikhululuka

zosindikizidwa

(Salimo 86:5)

  1. 1. Mwachikondi M’lungu

    Anapereka Yesu

    Kuti tikhululukidwe,

    Ndi kuthetsanso imfa.

    M’lungu amakhululuka,

    Ngati ife talapa.

    Nsembe ya dipo ya Yesu,

    Imatithandizadi.

  2. 2. Tikamatsanzira

    Chifundo cha Yehova

    Pokhululukira ena,

    Tidzakhululukidwa.

    Tikhale ololerana,

    Ndipo tisamadane;

    Tizilemekeza ena,

    Komanso kuwakonda.

  3. 3. Chifundo n’chabwino

    Tonse tikhale nacho.

    Sitidzasunga zifukwa,

    Tikakhumudwitsidwa.

    Tikatsanzira Yehova,

    Yemwe ndi wachikondi,

    Tidzakhululukirana;

    Tidzafanana naye.

(Onaninso Mat. 6:12; Aef. 4:32; Akol. 3:13.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani