Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 30
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 30:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:27; 28:2
  • +De 11:28; 28:15
  • +1Mf 8:47; Ne 1:9; Eze 18:28; Yow 2:13
  • +2Mf 17:6, 23; 25:26; 2Mb 36:20

Deuteronomo 30:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 55:7; Ho 3:5; 1Yo 1:9
  • +De 4:29

Deuteronomo 30:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 29:14
  • +Mlr 3:22
  • +Eza 1:3; Sl 147:2; Yes 56:8; Yer 32:37; Eze 34:13

Deuteronomo 30:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:64; Yes 11:11; Zef 3:20; Zek 8:7

Deuteronomo 30:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ne 1:9

Deuteronomo 30:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:16; Aro 2:29
  • +Yer 32:39
  • +De 6:5

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2007, tsa. 13

Deuteronomo 30:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 12:3; Yes 10:12; Yer 25:12; Mlr 3:64; Aro 12:19

Deuteronomo 30:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 30:2

Deuteronomo 30:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 65:21; Mki 3:10; Mt 6:33; Afi 4:19
  • +De 7:14; 28:4; Sl 107:38
  • +Le 26:4; Sl 67:6; 2Ak 9:10
  • +De 15:4; Miy 10:22
  • +De 28:63; Yer 32:41

Deuteronomo 30:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 26:17; 30:2
  • +Ne 1:9; Eze 18:21; 33:11; Mac 3:19

Deuteronomo 30:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 147:19; Miy 2:4; Yes 45:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/1/2009, tsa. 31

Deuteronomo 30:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 10:6

Deuteronomo 30:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 10:8
  • +Mt 7:21; Yak 1:25

Deuteronomo 30:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:26; 32:47

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/1/2009, tsa. 31

Deuteronomo 30:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:5; 30:6
  • +Miy 19:16; 1Ak 7:19
  • +Le 25:18; De 4:45; Sl 19:9
  • +Le 18:5; Ne 9:29; Aga 3:12
  • +De 30:5

Deuteronomo 30:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:18; 1Sa 12:25; Ahe 3:12
  • +De 4:19; 31:29; Sl 96:5

Deuteronomo 30:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 8:19; Yos 23:15

Deuteronomo 30:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:26; 28:2
  • +De 27:26; 28:15
  • +De 32:47
  • +De 4:26; 31:28; Yes 1:2
  • +De 6:2; Yer 32:39
  • +Yos 24:15

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Nsanja ya Olonda (Yogawira),

    No. 2 2018, tsatsa. 14-15

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/2010, tsa. 28

    6/1/2006, tsa. 27

    7/15/1999, ptsa. 11-12

    6/15/1996, ptsa. 12-17

    Galamukani!,

    2/2009, tsa. 13

Deuteronomo 30:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:12
  • +De 4:4
  • +De 4:40
  • +Ge 12:7; 15:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Nsanja ya Olonda (Yogawira),

    No. 2 2018, tsatsa. 14-15

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/2010, tsa. 28

    11/1/2009, tsa. 31

    6/1/2006, ptsa. 28-29

    7/15/1999, ptsa. 11-12

    Galamukani!,

    2/2009, tsa. 13

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 30:1De 11:27; 28:2
Deut. 30:1De 11:28; 28:15
Deut. 30:11Mf 8:47; Ne 1:9; Eze 18:28; Yow 2:13
Deut. 30:12Mf 17:6, 23; 25:26; 2Mb 36:20
Deut. 30:2Yes 55:7; Ho 3:5; 1Yo 1:9
Deut. 30:2De 4:29
Deut. 30:3Yer 29:14
Deut. 30:3Mlr 3:22
Deut. 30:3Eza 1:3; Sl 147:2; Yes 56:8; Yer 32:37; Eze 34:13
Deut. 30:4De 28:64; Yes 11:11; Zef 3:20; Zek 8:7
Deut. 30:5Ne 1:9
Deut. 30:6De 10:16; Aro 2:29
Deut. 30:6Yer 32:39
Deut. 30:6De 6:5
Deut. 30:7Ge 12:3; Yes 10:12; Yer 25:12; Mlr 3:64; Aro 12:19
Deut. 30:8De 30:2
Deut. 30:9Yes 65:21; Mki 3:10; Mt 6:33; Afi 4:19
Deut. 30:9De 7:14; 28:4; Sl 107:38
Deut. 30:9Le 26:4; Sl 67:6; 2Ak 9:10
Deut. 30:9De 15:4; Miy 10:22
Deut. 30:9De 28:63; Yer 32:41
Deut. 30:10De 26:17; 30:2
Deut. 30:10Ne 1:9; Eze 18:21; 33:11; Mac 3:19
Deut. 30:11Sl 147:19; Miy 2:4; Yes 45:19
Deut. 30:12Aro 10:6
Deut. 30:14Aro 10:8
Deut. 30:14Mt 7:21; Yak 1:25
Deut. 30:15De 11:26; 32:47
Deut. 30:16De 6:5; 30:6
Deut. 30:16Miy 19:16; 1Ak 7:19
Deut. 30:16Le 25:18; De 4:45; Sl 19:9
Deut. 30:16Le 18:5; Ne 9:29; Aga 3:12
Deut. 30:16De 30:5
Deut. 30:17De 29:18; 1Sa 12:25; Ahe 3:12
Deut. 30:17De 4:19; 31:29; Sl 96:5
Deut. 30:18De 8:19; Yos 23:15
Deut. 30:19De 11:26; 28:2
Deut. 30:19De 27:26; 28:15
Deut. 30:19De 32:47
Deut. 30:19De 4:26; 31:28; Yes 1:2
Deut. 30:19De 6:2; Yer 32:39
Deut. 30:19Yos 24:15
Deut. 30:20De 10:12
Deut. 30:20De 4:4
Deut. 30:20De 4:40
Deut. 30:20Ge 12:7; 15:18
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 30:1-20

Deuteronomo

30 “Ndiyeno zikadzachitika kuti mawu onsewa akwaniritsidwa pa inu, madalitso+ ndi matemberero+ amene ndakuikirani pamaso panu, ndipo mwakumbukira mawu amenewa mumtima mwanu+ muli pakati pa mitundu yonse kumene Yehova Mulungu wanu adzakubalalitsirani,+ 2 moti mwabwerera kwa Yehova Mulungu wanu+ ndi kumvera mawu ake ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse,+ mogwirizana ndi zonse zimene ndikukulamulani lero, inuyo ndi ana anu, 3 Yehova Mulungu wanu adzabweza kwawo anthu a mtundu wanu amene anagwidwa ndi kupita kudziko lina,+ ndipo adzakumverani chifundo+ n’kukusonkhanitsaninso pamodzi kuchokera pakati pa anthu onse kumene Yehova Mulungu wanu anakubalalitsirani.+ 4 Anthu a mtundu wanu obalalitsidwawo akadzakhala kumalekezero kwa thambo, Yehova Mulungu wanu adzakusonkhanitsani ndi kukutengani kumeneko.+ 5 Choncho Yehova Mulungu wanu adzakulowetsanidi m’dziko limene makolo anu analitenga kukhala lawo, ndipo inu mudzalitenga kukhala lanu. Pamenepo, adzakuchitirani zabwino ndi kukuchulukitsani kuposa makolo anu.+ 6 Yehova Mulungu wanu adzachita mdulidwe wa mitima yanu+ ndi mitima ya ana anu,+ kuti muzikonda Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse, kuti mukhale ndi moyo.+ 7 Ndipo Yehova Mulungu wanu adzaikadi matemberero onsewa pa adani anu, ndi onse odana ndi inu amene anakuzunzani.+

8 “Koma iwe udzatembenuka ndi kumvera mawu a Yehova ndi kutsatira malamulo ake onse amene ndikukupatsa lero.+ 9 Ndipo Yehova Mulungu wako adzakuchititsa kukhala ndi zinthu zosefukira pa ntchito iliyonse ya manja ako,+ chipatso cha mimba yako, chipatso cha ziweto zako+ ndi chipatso cha nthaka yako.+ Pamenepo udzatukuka+ chifukwa Yehova adzakondweranso nawe kuti akuchitire zabwino, monga mmene anakondwera ndi makolo ako.+ 10 Adzachita zimenezi popeza udzamvera mawu a Yehova Mulungu wako ndi kusunga malamulo ake ndi mfundo zake zolembedwa m’buku ili la chilamulo,+ chifukwa udzabwerera kwa Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse ndi moyo wako wonse.+

11 “Lamulo limene ndikukupatsa lero si lovuta kwa iwe kulitsatira, ndipo si lapatali.+ 12 Silili kumwamba kuti unene kuti, ‘Ndani adzakwera kumwamba ndi kukatitengera lamulolo kuti ife tilimve ndi kulitsatira?’+ 13 Ndiponso silili tsidya lina la nyanja kuti unene kuti, ‘Ndani adzawoloka kupita tsidya lina la nyanja kukatitengera lamulolo kuti ife tilimve ndi kulitsatira?’ 14 Pakuti mawu a chilamulowo ali pafupi kwambiri ndi iwe, ali m’kamwa mwako ndi mumtima mwako+ kuti uwatsatire.+

15 “Taona, ine ndikuika pamaso pako lero moyo ndi zinthu zabwino, imfa ndi zinthu zoipa.+ 16 [Ngati udzamvera malamulo a Yehova Mulungu wako,] amene ndikukupatsa lero ndi kukonda Yehova Mulungu wako,+ kuyenda m’njira zake ndi kusunga malamulo ake,+ mfundo zake ndi zigamulo zake,+ pamenepo udzakhaladi ndi moyo+ ndi kuchulukana. Ndipo Yehova Mulungu wako adzakudalitsa m’dziko limene ukupita kukalitenga kukhala lako.+

17 “Koma mtima wako ukatembenukira kwina ndipo sukumvera,+ moti wanyengeka, n’kugwadira milungu ina ndi kuitumikira,+ 18 ndikukuuzani lero kuti mudzatheratu.+ Simudzatalikitsa masiku anu panthaka imene mukupita kukaitenga kukhala yanu mutawoloka Yorodano. 19 Ndaika moyo ndi imfa, dalitso+ ndi temberero+ pamaso panu.+ Kumwamba ndi dziko lapansi ndi mboni pa zochita zanu.+ Choncho inuyo ndi mbadwa zanu+ musankhe moyo kuti mukhalebe ndi moyo.+ 20 Musankhe moyo mwa kukonda Yehova Mulungu wanu,+ kumvera mawu ake ndi kum’mamatira,+ chifukwa iye ndiye wokupatsani moyo ndi masiku ambiri+ kuti mukhale panthaka imene Yehova analumbira kwa makolo anu, Abulahamu, Isaki ndi Yakobo kuti adzawapatsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena