Genesis 25:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Anyamatawa anakula, ndipo Esau anakhala munthu wodziwa kusaka,+ munthu wokonda kuyenda m’tchire. Koma Yakobo anali kukhala nthawi yambiri m’mahema.+ Iye anali munthu wosalakwa.+ Genesis 27:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Zitatero, Rabeka anatenga zovala zokongola koposa za mwana wake wamkulu Esau,+ zimene anali nazo m’nyumba.+ Zovalazo anaveka mwana wake wamng’ono, Yakobo.+ Nyimbo ya Solomo 4:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Milomo yako imangokhalira kukha uchi wapachisa,+ iwe mkwatibwi wanga. Uchi+ ndi mkaka zili kuseri kwa lilime lako, ndipo kununkhira kwa zovala zako kuli ngati kununkhira+ kwa nkhalango ya Lebanoni.
27 Anyamatawa anakula, ndipo Esau anakhala munthu wodziwa kusaka,+ munthu wokonda kuyenda m’tchire. Koma Yakobo anali kukhala nthawi yambiri m’mahema.+ Iye anali munthu wosalakwa.+
15 Zitatero, Rabeka anatenga zovala zokongola koposa za mwana wake wamkulu Esau,+ zimene anali nazo m’nyumba.+ Zovalazo anaveka mwana wake wamng’ono, Yakobo.+
11 Milomo yako imangokhalira kukha uchi wapachisa,+ iwe mkwatibwi wanga. Uchi+ ndi mkaka zili kuseri kwa lilime lako, ndipo kununkhira kwa zovala zako kuli ngati kununkhira+ kwa nkhalango ya Lebanoni.