Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 42:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo iwo anati: “Akapolo anufe tilipo 12 pa ubale wathu.+ Ndife ana a munthu mmodzi amene akukhala ku Kanani.+ Wamng’ono kwambiri watsala ndi bambo athu,+ koma winayo kulibenso.”+

  • Genesis 43:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma iwo anayankha kuti: “Munthuyo anachita kufunsa za ife ndi banja lathu kuti, ‘Kodi bambo anu akali ndi moyo?+ Kodi muli ndi m’bale wanu wina?’ Ndipo ife tinayankha mogwirizana ndi zimene anafunsa.+ Nanga tikanadziwa bwanji zoti anena kuti, ‘Mukam’bweretse kuno m’bale wanuyo’?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena