Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Yehova Mulungu wanu akadzawakankhira kutali ndi inu musadzanene mumtima mwanu kuti, ‘Yehova watilowetsa m’dziko lino kuti tilitenge kukhala lathu, chifukwa cha kulungama kwathu,’+ pamene kwenikweni Yehova akukankhira mitundu iyi kutali ndi inu chifukwa cha kuipa kwawo.+

  • Salimo 80:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Munachititsa mtengo wa mpesa kuchoka mu Iguputo.+

      Munapitikitsa mitundu ya anthu kuti mubzalemo mtengowo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena