Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 26:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndiyeno uwombe nsalu yotchinga+ khomo la chihema. Nsaluyo ikhale ya ulusi wabuluu, ya ubweya wa nkhosa wonyika mu utoto wofiirira, ya ulusi wofiira kwambiri, ndi ya ulusi wopota wabwino kwambiri.

  • Ekisodo 40:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Atatero anakoloweka nsalu yotchinga+ pakhomo la chihema chopatulika.

  • Levitiko 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno usonkhanitse khamu lonse+ pakhomo la chihema chokumanako.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena