Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nditayang’ana, ndinaona kuti mwachimwira Yehova Mulungu wanu. Munali mutadzipangira mwana wa ng’ombe wachitsulo chosungunula.+ Munali mutapatuka mofulumira panjira imene Yehova anakulamulani kuyendamo.+

  • Nehemiya 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamene anasungunula chitsulo n’kudzipangira chifanizo cha mwana wa ng’ombe+ n’kuyamba kunena kuti, ‘Uyu ndiye Mulungu wanu, Aisiraeli inu, amene anakutulutsani mu Iguputo,’+ ndipo anachita zinthu zikuluzikulu zosakulemekezani,

  • Salimo 106:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Iwo anapanganso mwana wa ng’ombe ku Horebe,+

      Ndipo anaweramira chifaniziro chopangidwa ndi chitsulo chosungunula.+

  • Machitidwe 7:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Choncho iwo anapanga mwana wa ng’ombe m’masiku amenewo,+ ndi kubweretsa nsembe kwa fano limenelo. Pamenepo anasangalala ndi ntchito za manja awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena