Ekisodo 18:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Motero iwo anali kuweruza anthuwo pa nkhani iliyonse yoyenera. Nkhani yovuta anali kupita nayo kwa Mose,+ koma nkhani iliyonse yaing’ono, iwo monga oweruza anali kuisamalira. Numeri 27:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pamenepo, Mose anapereka dandaulo lawolo pamaso pa Yehova.+
26 Motero iwo anali kuweruza anthuwo pa nkhani iliyonse yoyenera. Nkhani yovuta anali kupita nayo kwa Mose,+ koma nkhani iliyonse yaing’ono, iwo monga oweruza anali kuisamalira.