Genesis 11:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Kenako anauzana kuti: “Tiyeni tiumbe njerwa tiziotche.” Atatero, anayamba kumanga ndi njerwa, n’kumagwiritsa ntchito phula ngati matope omangira.+ Genesis 19:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Ndiyeno anayang’ana kumunsi ku Sodomu ndi Gomora ndi kudera lonse la Chigawocho, ndipo anaona zoopsa. Kumeneko chiutsi chinali tolo! Chinali kufuka ngati chiutsi chochokera pa uvuni wa njerwa.+
3 Kenako anauzana kuti: “Tiyeni tiumbe njerwa tiziotche.” Atatero, anayamba kumanga ndi njerwa, n’kumagwiritsa ntchito phula ngati matope omangira.+
28 Ndiyeno anayang’ana kumunsi ku Sodomu ndi Gomora ndi kudera lonse la Chigawocho, ndipo anaona zoopsa. Kumeneko chiutsi chinali tolo! Chinali kufuka ngati chiutsi chochokera pa uvuni wa njerwa.+