Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 16:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Dziwani kuti Yehova wakupatsani sabata.+ N’chifukwa chake akukupatsani mkate wa masiku awiri pa tsiku la 6. Pa tsiku la 7 aliyense azikhala pamalo ake.+ Munthu asachoke pamalo ake.”

  • Deuteronomo 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma tsiku la 7 ndi sabata la Yehova Mulungu wako.+ Usagwire ntchito iliyonse,+ iweyo kapena mwana wako wamwamuna, mwana wako wamkazi, kapolo wako wamwamuna, kapolo wako wamkazi, ng’ombe yako yamphongo, bulu wako, chiweto chako chilichonse, kapena mlendo wokhala mumzinda wanu,+ kuti nayenso kapolo wako wamwamuna ndi kapolo wako wamkazi, azipumula monga iwe.+

  • Nehemiya 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu a ku Turo+ anali kukhala mumzindawo ndipo anali kubweretsa nsomba ndi malonda osiyanasiyana.+ Iwo anali kugulitsa zinthu zimenezi pa tsiku la sabata kwa ana a Yuda mu Yerusalemu.

  • Yohane 7:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ngati munthu amadulidwa tsiku la sabata posafuna kuphwanya chilamulo cha Mose, kodi mukundipsera mtima ine chifukwa ndinachiritsa munthu tsiku la sabata?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena