Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 139:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Maso anu anandiona pamene ndinali mluza,+

      Ndipo ziwalo zanga zonse zinalembedwa m’buku lanu.

      M’bukumo munalembamo za masiku amene zinapangidwa+

      Koma panalibe ngakhale chiwalo chimodzi chimene chinali chitapangidwa.

  • Yeremiya 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Ndisanakuumbe m’mimba,+ ndinakudziwa,+ ndipo usanatuluke m’mimbamo, ndinakusankha kuti uchite ntchito yopatulika.+ Ndinakusankha kuti ukhale mneneri ku mitundu ya anthu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena