Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma chaka cha 7 usaulime, uusiye kuti ugonere.+ Osauka mwa anthu ako adye za m’mundamo ndipo zimene iwo asiya, zilombo zakutchire zidye.+ Uzichita zimenezi ndi munda wako wa mpesa ndi wa maolivi.

  • Levitiko 25:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndipo inuyo, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi, waganyu wanu, mlendo wokhaliratu amene akukhala pakati panu, ndi alendo ena okhala m’nyumba mwanu, muzidya zimene zamera m’chaka cha sabatacho.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena