Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno masiku a kuyeretsedwa kwake chifukwa chobereka mwana wamwamuna kapena wamkazi akakwana, azibweretsa kwa wansembe, pakhomo la chihema chokumanako, nkhosa yaing’ono yamphongo yosapitirira chaka chimodzi kuti ikhale nsembe yopsereza.+ Azibweretsanso mwana wa nkhunda kapena njiwa+ kuti ikhale nsembe yamachimo.

  • Numeri 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 popereka nsembe yotentha ndi moto kwa Yehova,+ kuti ikhale nsembe yopsereza,+ kapena nsembe yochitira lonjezo lapadera, kapena nsembe yongopereka mwaufulu,+ kapena yopereka pa nthawi ya zikondwerero zanu,+ kuti mufukize fungo lokhazika mtima pansi kwa Yehova+ la nyama ya ng’ombe kapena ya nkhosa,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena