Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 21:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Potsirizira pake, madzi anamuthera+ m’thumba lachikopa lija, ndipo iye anangomusiya+ mwana uja pachitsamba.

  • Levitiko 13:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 “Koma wansembeyo akaona, n’kupeza kuti nthendayo sinafalikire pachovalacho, m’litali kapena m’lifupi, kapena pa chilichonse chopangidwa ndi chikopa,+

  • Maliko 2:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiponso, palibe munthu amene amathira vinyo watsopano m’matumba achikopa akale. Akachita zimenezo, vinyoyo amaphulitsa matumbawo. Kenako vinyoyo amatayika ndipo matumbawo amawonongeka.+ Koma anthu amathira vinyo watsopano m’matumba achikopa atsopano.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena