Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 33:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndipo kwa Levi anati:+

      “Tumimu ndi Urimu+ wanu ndizo za munthu wokhulupirika kwa inu,+

      Amene munamuyesa pa Masa.+

      Munayamba kulimbana naye pafupi ndi madzi a Meriba.+

  • Salimo 95:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Musaumitse mitima yanu monga mmene makolo anu anachitira pa Meriba,+

      Monga mmene anachitira pa Masa m’chipululu,+

  • Salimo 106:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kuwonjezera pamenepo, iwo anaputa mkwiyo pa madzi a ku Meriba,+

      Moti Mose sizinamuyendere bwino chifukwa cha anthu amenewa.+

  • Aheberi 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 musaumitse mitima yanu ngati mmene zinakhalira pamene makolo anu anandipsetsa mtima,+ ngati mmene zinalili pa tsiku la mayeso+ m’chipululu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena