Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 1:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 Alevi azimanga mahema awo mozungulira chihema cha Umboni kuti mkwiyo+ wa Mulungu usawayakire ana a Isiraeli. Aleviwo azitumikira pachihema cha Umbonicho.”+

  • Numeri 3:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Mkulu wa atsogoleri onse a Alevi anali Eleazara,+ mwana wa wansembe Aroni. Iye ndiye anali kuyang’anira onse otumikira pamalo oyera.

  • Numeri 18:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Azikhala pafupi nanu kuti azichita utumiki wawo wonse wa pachihema chokumanako, ndipo munthu wina aliyense amene si Mlevi asayandikire kwa inu.+

  • 1 Mbiri 23:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ana a Leviwa analinso ndi ntchito yolondera+ chihema chokumanako, malo oyera,+ ndiponso yolondera abale awo, ana a Aroni, pa utumiki wa panyumba ya Yehova.+

  • Ezekieli 44:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Aleviwo adzakhala atumiki m’malo anga opatulika. Adzakhala ndi maudindo oyang’anira zipata za Nyumba ino ndipo adzakhala atumiki a pa Nyumbayi.+ Iwo azidzapha nyama za nsembe yopsereza yathunthu ndi nsembe zina za anthu+ ndipo adzaimirira pamaso pa anthuwo ndi kuwatumikira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena