Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Anauza Mose kuti: “Tinakalowa m’dziko limene munatitumako. Ndithudi ndi dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ ndipo zipatso zake ndi izi.+

  • Deuteronomo 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Motero anatengako zina mwa zipatso za m’dzikolo+ ndi kutibweretsera. Iwo anatiuza kuti, ‘Dziko limene Yehova Mulungu wathu akutipatsa ndi labwino.’+

  • Deuteronomo 8:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pakuti Yehova Mulungu wanu akukulowetsani m’dziko labwino,+ dziko la zigwa* za madzi,+ akasupe ndi madzi ochuluka otuluka m’zigwa ndi m’madera a mapiri,

  • Deuteronomo 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 iyenso* adzakupatsani mvula pa nthawi yake m’dziko lanu,+ mvula yoyambirira ndi mvula yomaliza,+ ndipo mudzakololadi mbewu zanu ndi kukhaladi ndi vinyo wotsekemera* komanso mafuta.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena