-
Rute 4:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Poyankha wowombolayo anati: “Sinditha kuuwombola, kuopera kuti ndingawononge cholowa changa. Iweyo uuwombole m’malo mwa ine, chifukwa ine sinditha kuuwombola.”
-