Levitiko 20:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 N’chifukwa chake ndinakuuzani+ kuti: “Inuyo mudzatenga dzikolo ndipo ine ndidzalipereka m’manja mwanu kuti likhale lanu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndakupatulani kwa anthu a mitundu ina.”+ Numeri 13:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Anauza Mose kuti: “Tinakalowa m’dziko limene munatitumako. Ndithudi ndi dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ ndipo zipatso zake ndi izi.+ Numeri 14:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Yehova akatikomera mtima,+ ndithu adzatilowetsa m’dzikolo n’kulipereka kwa ife, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Deuteronomo 26:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndiyeno anatibweretsa kumalo ano ndi kutipatsa dziko ili, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Yeremiya 11:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 kuti ndikwaniritse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu+ kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene zilili lero.’”’” Pamenepo ine ndinayankha kuti: “Zikhale momwemo,* inu Yehova.” Yeremiya 32:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 “Patapita nthawi munawapatsa dziko lino, limene munalumbirira makolo awo kuti mudzawapatsa,+ dziko loyenda mkaka ndi uchi.+
24 N’chifukwa chake ndinakuuzani+ kuti: “Inuyo mudzatenga dzikolo ndipo ine ndidzalipereka m’manja mwanu kuti likhale lanu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndakupatulani kwa anthu a mitundu ina.”+
27 Anauza Mose kuti: “Tinakalowa m’dziko limene munatitumako. Ndithudi ndi dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ ndipo zipatso zake ndi izi.+
8 Yehova akatikomera mtima,+ ndithu adzatilowetsa m’dzikolo n’kulipereka kwa ife, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+
5 kuti ndikwaniritse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu+ kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene zilili lero.’”’” Pamenepo ine ndinayankha kuti: “Zikhale momwemo,* inu Yehova.”
22 “Patapita nthawi munawapatsa dziko lino, limene munalumbirira makolo awo kuti mudzawapatsa,+ dziko loyenda mkaka ndi uchi.+