Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 20:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 N’chifukwa chake ndinakuuzani+ kuti: “Inuyo mudzatenga dzikolo ndipo ine ndidzalipereka m’manja mwanu kuti likhale lanu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndakupatulani kwa anthu a mitundu ina.”+

  • Numeri 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Anauza Mose kuti: “Tinakalowa m’dziko limene munatitumako. Ndithudi ndi dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ ndipo zipatso zake ndi izi.+

  • Numeri 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yehova akatikomera mtima,+ ndithu adzatilowetsa m’dzikolo n’kulipereka kwa ife, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+

  • Deuteronomo 26:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno anatibweretsa kumalo ano ndi kutipatsa dziko ili, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+

  • Yeremiya 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 kuti ndikwaniritse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu+ kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene zilili lero.’”’”

      Pamenepo ine ndinayankha kuti: “Zikhale momwemo,* inu Yehova.”

  • Yeremiya 32:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Patapita nthawi munawapatsa dziko lino, limene munalumbirira makolo awo kuti mudzawapatsa,+ dziko loyenda mkaka ndi uchi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena