Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pambuyo pake Yehova anauza Mose ndi Aroni kuti: “Chifukwa simunasonyeze chikhulupiriro mwa ine, polephera kundilemekeza+ pamaso pa ana a Isiraeli, simudzaulowetsa mpingowu m’dziko limene ndidzawapatse.”+

  • Deuteronomo 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kwera pamwamba pa Pisiga+ ndi kukweza maso ako, ndipo uyang’ane kumadzulo, kumpoto, kum’mwera ndi kum’mawa, uone dzikolo ndi maso ako, chifukwa suwoloka Yorodano uyu.+

  • Deuteronomo 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Ndipo Yehova anandikwiyira chifukwa cha inu,+ kotero kuti analumbira kuti ndisawoloke Yorodano, kapena kulowa m’dziko labwino limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kukhala cholowa chanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena