Numeri 14:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 sadzaliona m’pang’ono pomwe dziko limene ndinalumbirira makolo awo. Ndithudi, onse amene sakundipatsa ulemu, sadzaliona dzikolo.+ Deuteronomo 1:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 ‘Palibe munthu ndi mmodzi yemwe mwa anthu a m’badwo woipa uwu amene adzaona dziko labwino limene ndinalumbira kuti ndidzalipereka kwa makolo anu,+ Salimo 106:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Choncho Mulungu anawalumbirira atakweza dzanja lake,+Kuti adzawapha m’chipululu,+
23 sadzaliona m’pang’ono pomwe dziko limene ndinalumbirira makolo awo. Ndithudi, onse amene sakundipatsa ulemu, sadzaliona dzikolo.+
35 ‘Palibe munthu ndi mmodzi yemwe mwa anthu a m’badwo woipa uwu amene adzaona dziko labwino limene ndinalumbira kuti ndidzalipereka kwa makolo anu,+