Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Tamverani Aisiraeli inu, lero mukuwoloka Yorodano+ kulowa m’dziko limene mukukalilanda kwa mitundu ikuluikulu ndi yamphamvu kuposa inuyo.+ Mukukalanda mizinda ikuluikulu yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri yofika kumwamba.+

  • Deuteronomo 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Pakuti mukuwoloka Yorodano ndi kukalowa m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti mulitenge kukhala lanu. Mukalitengedi ndi kukhala momwemo.+

  • Yoswa 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Patatha masiku atatu aja,+ akapitawo+ a anthuwo anapita mumsasa,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena