Ekisodo 14:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Iye anali kugulula mawilo a magaleta awo moti anali kuwayendetsa movutikira.+ Pamenepo Aiguputo anayamba kunena kuti: “Tiyeni tithawe pamaso pa Isiraeli, chifukwa Yehova akuwamenyera nkhondo yolimbana ndi Aiguputo.”+ Deuteronomo 28:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 “Yehova adzachititsa adani ako amene adzakuukira kugonja pamaso pako.+ Pobwera kwa iwe adzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso pako, adzadutsa njira 7.+ 2 Mafumu 7:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Nthawi yomweyo anthuwo ananyamuka n’kuyamba kuthawa kukungoyamba kumene kuda.+ Anasiya mahema awo, mahatchi awo,+ ndi abulu awo. Msasawo anausiya mmene unalili n’kuthawa kuti apulumutse miyoyo yawo.+
25 Iye anali kugulula mawilo a magaleta awo moti anali kuwayendetsa movutikira.+ Pamenepo Aiguputo anayamba kunena kuti: “Tiyeni tithawe pamaso pa Isiraeli, chifukwa Yehova akuwamenyera nkhondo yolimbana ndi Aiguputo.”+
7 “Yehova adzachititsa adani ako amene adzakuukira kugonja pamaso pako.+ Pobwera kwa iwe adzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso pako, adzadutsa njira 7.+
7 Nthawi yomweyo anthuwo ananyamuka n’kuyamba kuthawa kukungoyamba kumene kuda.+ Anasiya mahema awo, mahatchi awo,+ ndi abulu awo. Msasawo anausiya mmene unalili n’kuthawa kuti apulumutse miyoyo yawo.+