Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Tsopano Sarai, mkazi wa Abulamu, sanamuberekere ana.+ Koma Saraiyo anali ndi kapolo wake Mwiguputo, dzina lake Hagara.+

  • Genesis 25:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Isaki anali kupembedzera Yehova mosalekeza, makamaka chifukwa cha mkazi wake,+ popeza iye anali wosabereka.+ Yehova anamva kupembedzera kwake,+ ndipo Rabeka mkazi wakeyo anakhala ndi pakati.

  • Luka 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma iwo analibe mwana, chifukwa Elizabeti anali wosabereka,+ ndipo onse awiri anali okalamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena