Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iye anayankha kuti: “Ndidzakutumizira mwana wa mbuzi.” Koma mkaziyo anati: “Mundipatse chikole choti ndisunge kufikira pamene mudzaitumize.”+

  • 1 Samueli 16:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pamenepo Jese anatenga bulu, mkate, thumba lachikopa+ la vinyo ndi mwana wa mbuzi, ndipo anazitumiza kwa Sauli kudzera mwa Davide mwana wake.+

  • Luka 15:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Poyankha iye anauza bambo akewo kuti, ‘Ine zaka zonsezi ndakhala ndikukugwirirani ntchito ngati kapolo, ndipo sindinaphwanyepo malamulo anu n’kamodzi komwe, koma simunandipatseko ngakhale kamwana ka mbuzi kuti ndisangalale ndi mabwenzi anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena