Rute 2:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndiyeno Boazi anamuyankha kuti: “Ndamva zonse zimene wachitira apongozi ako chimwalilireni mwamuna wako.+ Ndamvanso kuti unasiya bambo ako ndi mayi ako, komanso dziko la abale ako, n’kubwera kuno kwa anthu amene sunali kuwadziwa n’kale lonse.+ Esitere 8:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 M’zigawo zonse ndi m’mizinda yonse kumene mawu a mfumu ndi lamulo lake linafika, Ayuda anali kusangalala ndi kukondwera. Anachita phwando+ ndipo linali tsiku lachisangalalo. Anthu ambiri+ a m’dzikomo anayamba kudzitcha Ayuda+ chifukwa anali kuchita mantha kwambiri+ ndi Ayudawo. Salimo 45:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Iwe mwana wanga wamkazi, mvetsera ndipo ona ndi kutchera khutu.Uiwale anthu ako ndi nyumba ya bambo ako.+ Yesaya 14:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pakuti Yehova adzachitira chifundo Yakobo+ ndipo adzasankhanso Isiraeli.+ Iye adzawapatsa mpumulo m’dziko lawo.+ Alendo adzakhala nawo limodzi ndipo adzadziphatika kunyumba ya Yakobo.+
11 Ndiyeno Boazi anamuyankha kuti: “Ndamva zonse zimene wachitira apongozi ako chimwalilireni mwamuna wako.+ Ndamvanso kuti unasiya bambo ako ndi mayi ako, komanso dziko la abale ako, n’kubwera kuno kwa anthu amene sunali kuwadziwa n’kale lonse.+
17 M’zigawo zonse ndi m’mizinda yonse kumene mawu a mfumu ndi lamulo lake linafika, Ayuda anali kusangalala ndi kukondwera. Anachita phwando+ ndipo linali tsiku lachisangalalo. Anthu ambiri+ a m’dzikomo anayamba kudzitcha Ayuda+ chifukwa anali kuchita mantha kwambiri+ ndi Ayudawo.
10 Iwe mwana wanga wamkazi, mvetsera ndipo ona ndi kutchera khutu.Uiwale anthu ako ndi nyumba ya bambo ako.+
14 Pakuti Yehova adzachitira chifundo Yakobo+ ndipo adzasankhanso Isiraeli.+ Iye adzawapatsa mpumulo m’dziko lawo.+ Alendo adzakhala nawo limodzi ndipo adzadziphatika kunyumba ya Yakobo.+