Levitiko 11:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Tizilombo timeneti n’timene mungadzidetse nato. Aliyense wokhudza zolengedwa zimenezi zitafa azikhala wodetsedwa kufikira madzulo.+ Levitiko 15:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Komanso munthu wokhudza bedi lakelo azichapa zovala zake ndi kusamba thupi lonse, ndipo azikhala wodetsedwa kufikira madzulo.+ Levitiko 15:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 “‘Mwamuna akatulutsa umuna,+ azisamba thupi lonse, ndipo azikhala wodetsedwa kufikira madzulo. Levitiko 15:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 “‘Mkazi akagonana ndi mwamuna, onse awiri azisamba thupi lonse, ndipo azikhala odetsedwa+ kufikira madzulo. Numeri 19:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Aliyense amene wakhudza mtembo wa munthu amene waphedwa ndi lupanga,+ kapena mtembo uliwonse, kapenanso fupa la munthu,+ ngakhalenso manda a munthu, akhale wodetsedwa masiku 7.
24 Tizilombo timeneti n’timene mungadzidetse nato. Aliyense wokhudza zolengedwa zimenezi zitafa azikhala wodetsedwa kufikira madzulo.+
5 Komanso munthu wokhudza bedi lakelo azichapa zovala zake ndi kusamba thupi lonse, ndipo azikhala wodetsedwa kufikira madzulo.+
18 “‘Mkazi akagonana ndi mwamuna, onse awiri azisamba thupi lonse, ndipo azikhala odetsedwa+ kufikira madzulo.
16 Aliyense amene wakhudza mtembo wa munthu amene waphedwa ndi lupanga,+ kapena mtembo uliwonse, kapenanso fupa la munthu,+ ngakhalenso manda a munthu, akhale wodetsedwa masiku 7.