Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 6:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Komabe, Gidiyoni anauza Mulungu woona kuti: “Mkwiyo wanu usandiyakire chonde, ndiloleni ndilankhulenso kamodzi kokhaka. Ndiloleni chonde, ndikuyeseninso kamodzi kokha ndi ubweyawu, kuti nditsimikizire za nkhaniyi. Nthaka yonse ikhathamire ndi mame, koma ubweya wokhawu ukhale wouma.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena