Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 54:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti pali anthu achilendo amene andiukira,

      Ndipo pali olamulira ankhanza amene akufuna moyo wanga.+

      Sanaike Mulungu patsogolo pawo.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 70:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Amene akufunafuna moyo wanga achite manyazi ndi kuthedwa nzeru.+

      Amene akukondwera ndi tsoka langa abwerere ndipo anyazitsidwe.+

  • Miyambo 29:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Anthu ambiri amafuna kuonana ndi mtsogoleri,+ koma chiweruzo cha munthu chimachokera kwa Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena