1 Samueli 13:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Kenako Samueli anati: “N’chiyani chimene wachita?”+ Poyankha Sauli anati: “Nditaona kuti anthu akubalalika kundisiya ndekha,+ ndipo inu simunabwere m’masiku amene munanena aja,+ komanso kuti Afilisiti anali kusonkhana pamodzi ku Mikimasi,+ 1 Mbiri 10:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Choncho Sauli anafa chifukwa cha kusakhulupirika kwake popeza anachita zosakhulupirika+ kwa Yehova. Iye sanasunge mawu a Yehova komanso anapita kukafunsa kwa wolankhula ndi mizimu.+
11 Kenako Samueli anati: “N’chiyani chimene wachita?”+ Poyankha Sauli anati: “Nditaona kuti anthu akubalalika kundisiya ndekha,+ ndipo inu simunabwere m’masiku amene munanena aja,+ komanso kuti Afilisiti anali kusonkhana pamodzi ku Mikimasi,+
13 Choncho Sauli anafa chifukwa cha kusakhulupirika kwake popeza anachita zosakhulupirika+ kwa Yehova. Iye sanasunge mawu a Yehova komanso anapita kukafunsa kwa wolankhula ndi mizimu.+